MCP National Youth League

MCP National Youth League A Better and Prosperous Malawi is Possible (Nothing for Us without Us)
(1)

Mtsogoleri wa Zipani Zotsutsa M’nyumba ya Malamulo, a Simplex Chithyola Banda, wadzudzula boma chifukwa cholephera kutha...
16/06/2026

Mtsogoleri wa Zipani Zotsutsa M’nyumba ya Malamulo, a Simplex Chithyola Banda, wadzudzula boma chifukwa cholephera kuthana ndi mavuto a m’dziko muno moyenera, kuphatikizapo masautso omwe aMalawi omwe ali ku South Africa akukumana nawo komanso kukwera kwa mavuto azachuma.

M’chikalata chomwe atulutsa lero, a Banda apempha boma kuti lichitepo kanthu mwachangu pofuna kuthandiza nzika zomwe zili m’masautsozi.

Pa zogawanitsa Mtundu, iwo adzudzula zomwe adalankhula Nduna yowona ubale ndi maiko ena, a George Chaponda, zokhudza a Malawi amtundu wa Chingoni aku Mzimba, ndipo achenjeza kuti malankhulidwe oterewa akhoza kusokoneza mgwirizano ndi mtendere wa dziko.

A Banda awonetsa kukhudzidwa mtima kwambiri ndi zomwe zikuwoneka ngati njira zofuna kufooketsa komanso kuchepetsa ulamuliro wa Ofesi ya Wachiwiri kwa Purezidenti wa dziko lino.

Iwonso adzudzula kukwera kwa mchitidwe wosalolerana pa ndale, kugwiritsa ntchito molakwika mabungwe a boma, komanso mchitidwe wachibale (nepotism) pa ntchito za boma.

A Banda apempha atsogoleri a boma kuti aziyika patsogolo kukhala odalirika komanso owonekera poyera (accountability), ndikukhazikitsa ndondomeko zomwe zikuthandiza nzika poyamba, makamaka pa nthawi yomwe mitengo ya Katundu komanso kusowa kwa ntchito (ulova) zikukwera m'dziko muno.

𝐆𝐀𝐍𝐆𝐀𝐓𝐀 𝐀𝐍𝐘𝐀𝐍𝐘𝐀𝐋𝐀 𝐌𝐔𝐙𝐎𝐂𝐇𝐈𝐓𝐈𝐊𝐀 𝐙𝐀 𝐃𝐏𝐏 𝐌'𝐂𝐇𝐈𝐆𝐀𝐖𝐎 𝐂𝐇𝐀 𝐏𝐀𝐊𝐀𝐓𝐈. Wachiwiri kwa Purezidenti wa chipani cha Democratic Progressi...
10/06/2026

𝐆𝐀𝐍𝐆𝐀𝐓𝐀 𝐀𝐍𝐘𝐀𝐍𝐘𝐀𝐋𝐀 𝐌𝐔𝐙𝐎𝐂𝐇𝐈𝐓𝐈𝐊𝐀 𝐙𝐀 𝐃𝐏𝐏 𝐌'𝐂𝐇𝐈𝐆𝐀𝐖𝐎 𝐂𝐇𝐀 𝐏𝐀𝐊𝐀𝐓𝐈.

Wachiwiri kwa Purezidenti wa chipani cha Democratic Progressive Party (DPP) m'Chigawo cha Pakati, a Alfred Gangata, akuti anyanyala pazochitika a chipanichi m'chigawochi, kamba ka kusakhutira komwe kukukulirakulira ndi momwe atsogoleri apamwamba a chipanichi akuchitira zinthu naye.

Mboni zosiyanasiyana zikuwonetsa kuti a Gangata akuimba mlandu akuluakulu m'chipani cha DPP kuti ndi osayamika, ngakhale iwo akhala akuthandiza kwambiri chipanichi.

Iwo akutinso pakuchitika zoyesayesa zofuna kusokoneza mabizinesi awo. A Gangata adzipatula pazochitika zilizonse za chipanichi ndipo sakhudzidwanso nawo m'misonkhano ya DPP m'Chigawo cha pakati.

Kusapezeka kwawo kwadziwika kwambiri pamene chipani cha DPP chikuchititsa msonkhano ya campaign yolimbikitsa anthu pamaso pa zisankho zazing'ono (by-elections) zomwe zikubwera m'chigawochi.

Ngakhale ali wachiwiri kwa purezidenti wa chipanichi m'chigawochi, akuti a Gangata sanakhudzidwe nawo m'zochitika zandale komanso misonkhano ya campaign yaposachedwapa.

Anthu amkati mwa chipanichi akuti nkhaniyi yabweretsa nkhawa pakati pa mamembala ena, poganizira udindo waukulu womwe a Gangata ali nawo m'Chigawo cha Pakati komanso kusatenga nawo mbali kwanthawi yayitali m'zochitika zam'chipanichi.

Ukuku apwetekana basi

10/06/2026

This is what Namiwa is saying:

​He says, "People have lost faith in the Mkulukuta Moyo Government, and people are suffering under this Government more than ever before, anthu akungoyenda wapasi basi.

Central Medical Stores kuchita kuyigawana ma Banja awiri, a Chisale ndi a Mukhitho 😮‍💨
07/06/2026

Central Medical Stores kuchita kuyigawana ma Banja awiri, a Chisale ndi a Mukhitho 😮‍💨

𝐇𝐈𝐆𝐇 𝐂𝐎𝐔𝐑𝐓 𝐁𝐋𝐎𝐂𝐊𝐒 𝐏𝐑𝐄𝐒𝐈𝐃𝐄𝐍𝐓𝐈𝐀𝐋 𝐎𝐑𝐃𝐄𝐑 𝐓𝐎 𝐌𝐎𝐕𝐄 𝐌𝐄𝐂 𝐓𝐎 𝐁𝐋𝐀𝐍𝐓𝐘𝐑𝐄.The High Court in Lilongwe has blocked President Peter Muth...
05/06/2026

𝐇𝐈𝐆𝐇 𝐂𝐎𝐔𝐑𝐓 𝐁𝐋𝐎𝐂𝐊𝐒 𝐏𝐑𝐄𝐒𝐈𝐃𝐄𝐍𝐓𝐈𝐀𝐋 𝐎𝐑𝐃𝐄𝐑 𝐓𝐎 𝐌𝐎𝐕𝐄 𝐌𝐄𝐂 𝐓𝐎 𝐁𝐋𝐀𝐍𝐓𝐘𝐑𝐄.

The High Court in Lilongwe has blocked President Peter Mutharika’s October 2025 executive order to relocate the Malawi Electoral Commission (MEC) from Lilongwe to Blantyre.

Judge Kenyatta Nyirenda granted a temporary injunction alongside permission for a full judicial review. The legal challenge was launched by the opposition Malawi Congress Party (MCP) and three citizens: Emmanuel Chambulanyina Jere, Abraham Mwakhwawa, and Daniel Mwanyongo Chitonya.

According to the court order, the government and its agents are strictly restrained from taking "any further steps towards the relocation of the Malawi Electoral Commission... to Blantyre or to any other place whatsoever" until the matter is fully decided.

"With this Order, MEC will not be relocated," confirmed George Jivason Kadzipatike, the lawyer representing the petitioners.

The ruling temporarily halts the presidency's broader plan to move several key state agencies out of the capital.

𝐌𝐀𝐋𝐀𝐖𝐈 𝐃𝐀𝐍𝐆𝐄𝐑𝐎𝐔𝐒𝐋𝐘 𝐃𝐄𝐒𝐄𝐍𝐒𝐈𝐓𝐈𝐒𝐄𝐃 𝐓𝐎 𝐂𝐑𝐈𝐒𝐄𝐒 𝐔𝐍𝐃𝐄𝐑 𝐃𝐏𝐏 𝐆𝐎𝐕𝐓, 𝐖𝐀𝐑𝐍𝐒 𝐂𝐂𝐉𝐏The Catholic Commission for Justice and Peace says t...
05/06/2026

𝐌𝐀𝐋𝐀𝐖𝐈 𝐃𝐀𝐍𝐆𝐄𝐑𝐎𝐔𝐒𝐋𝐘 𝐃𝐄𝐒𝐄𝐍𝐒𝐈𝐓𝐈𝐒𝐄𝐃 𝐓𝐎 𝐂𝐑𝐈𝐒𝐄𝐒 𝐔𝐍𝐃𝐄𝐑 𝐃𝐏𝐏 𝐆𝐎𝐕𝐓, 𝐖𝐀𝐑𝐍𝐒 𝐂𝐂𝐉𝐏

The Catholic Commission for Justice and Peace says the country under DPP Government has become dangerously desensitised to crises.

In a statement issued on Friday, CCJP points to superstition killings, fake medicines, unresolved abductions, political cronyism, forex shortages and court delays stretching 28 years.

“The danger lies not only in these crises themselves, but in our growing acceptance of them as ordinary features of national life,” CCJP says.

The Commission recalls the mass hysteria in Chikwawa and Nsanje where “rumours surrounding the mysterious disappearance or alleged shrinking of male private parts triggered mass hysteria, panic and mob violence, resulting in the deaths of at least eight people.”

On medicines, CCJP reveals that expired insulin was allegedly re-labelled and distributed across key health facilities after being stolen from hospital storage, adding that a 2024 study by the Kamuzu University of Health Sciences shows that nearly 14 percent of essential medicines, including antibiotics, fail to meet required quality standards.

A court case that has taken more than 28 years involving Rodwell Zimba is described as a complete embarrassment to judicial integrity.

“We need to get out completely of the Bagamoyo situation as soon as possible,” CCJP says referring to the Bishops’ pastoral letter “The Sad Story of Malawi”.

CCJP also acknowledges government efforts on inflation and maize prices. But it says recovery needs an honest reckoning from all Malawians and not just leaders.

The Commission says competent public servants are being pushed aside while loyalists get jobs in state-owned enterprises and diplomatic missions. CCJP also calls on religious leaders and traditional healers to desist from fabricating and spreading false news that cause public panic and unnecessary community tensions.

𝐂𝐇𝐀𝐊𝐖𝐄𝐑𝐀 𝐈𝐍 𝐏𝐀𝐑𝐓𝐘 𝐒𝐓𝐑𝐄𝐍𝐆𝐓𝐇𝐄𝐍𝐈𝐍𝐆 𝐃𝐑𝐈𝐕𝐄. MCP President and 6th President of Malawi, Dr. Lazarus McCarthy Chakwera, today m...
04/06/2026

𝐂𝐇𝐀𝐊𝐖𝐄𝐑𝐀 𝐈𝐍 𝐏𝐀𝐑𝐓𝐘 𝐒𝐓𝐑𝐄𝐍𝐆𝐓𝐇𝐄𝐍𝐈𝐍𝐆 𝐃𝐑𝐈𝐕𝐄.

MCP President and 6th President of Malawi, Dr. Lazarus McCarthy Chakwera, today met with Hon. Nkhosa Kamwendo, one of the longest-serving members of the Malawi Congress Party, at MCP Headquarters in Lilongwe.

The meeting is part of the party's ongoing efforts to strengthen and consolidate, aimed at enhancing unity, engagement, and preparedness for future political activities.

Wishing a very happy birthday to the most capable Secretary General among all political parties in Malawi, Hon. Chimwend...
04/06/2026

Wishing a very happy birthday to the most capable Secretary General among all political parties in Malawi, Hon. Chimwendo Richard William Banda MP. Your tireless work and commitment inspire us all. Have a wonderful day and may God bless you.

𝐍𝐀𝐓𝐈𝐎𝐍 𝐏𝐔𝐁𝐋𝐈𝐂𝐀𝐓𝐈𝐎𝐍𝐒 𝐁𝐄𝐈𝐍𝐆 𝐔𝐒𝐄𝐃 𝐁𝐘 𝐃𝐏𝐏 𝐆𝐎𝐕𝐓 𝐓𝐎 𝐃𝐄𝐂𝐄𝐈𝐕𝐄 𝐌𝐀𝐋𝐀𝐖𝐈𝐀𝐍𝐒 People are calling out Nation Publications Limited  for ...
02/06/2026

𝐍𝐀𝐓𝐈𝐎𝐍 𝐏𝐔𝐁𝐋𝐈𝐂𝐀𝐓𝐈𝐎𝐍𝐒 𝐁𝐄𝐈𝐍𝐆 𝐔𝐒𝐄𝐃 𝐁𝐘 𝐃𝐏𝐏 𝐆𝐎𝐕𝐓 𝐓𝐎 𝐃𝐄𝐂𝐄𝐈𝐕𝐄 𝐌𝐀𝐋𝐀𝐖𝐈𝐀𝐍𝐒

People are calling out Nation Publications Limited for using an old photo on today's front page. The newspaper claimed the picture showed President Mutharika with his ministers after last week's Cabinet meeting.

However, internet users quickly proved the photo was actually taken months ago, on February 23, 2026, noting that the ministers are wearing completely different clothes.

Because no real group photos were released from last week's meeting, this mix-up has fueled rumors that the President didn't actually attend and that a minister chaired the session instead.

The public is now demanding to see a genuine photo from last week to prove what really happened.

Lies have short legs!

𝐃𝐏𝐏'𝐒 𝐁𝐈𝐓𝐓𝐄𝐑 𝐏𝐈𝐋𝐋: 𝐍𝐄𝐖 𝐓𝐀𝐗𝐄𝐒 𝐇𝐈𝐓 𝐌𝐀𝐋𝐀𝐑𝐈𝐀 𝐃𝐑𝐔𝐆𝐒 𝐀𝐍𝐃 𝐏𝐀𝐈𝐍 𝐊𝐈𝐋𝐋𝐄𝐑𝐒. The DPP Government has introduced new import duties on ...
30/05/2026

𝐃𝐏𝐏'𝐒 𝐁𝐈𝐓𝐓𝐄𝐑 𝐏𝐈𝐋𝐋: 𝐍𝐄𝐖 𝐓𝐀𝐗𝐄𝐒 𝐇𝐈𝐓 𝐌𝐀𝐋𝐀𝐑𝐈𝐀 𝐃𝐑𝐔𝐆𝐒 𝐀𝐍𝐃 𝐏𝐀𝐈𝐍 𝐊𝐈𝐋𝐋𝐄𝐑𝐒.

The DPP Government has introduced new import duties on several commonly used medicines, a move likely to increase the cost of treatment for ordinary Malawians.

A Malawi Revenue Authority (MRA) Customs and Excise Circular issued on 27 May 2026 shows that Amoxicillin 250mg capsules and 125mg dry suspension will now attract a 20 percent tariff, while Artemether-Lumefantrine (anti-malaria medicine), Paracetamol, Aspirin and Ibuprofen will attract a 25 percent tariff.

The tariff adjustments stem from customs and excise changes approved through the 2026/27 budget process.

The new measures are expected to increase the cost of importing these medicines, with importers likely to pass on the costs to consumers through higher prices in pharmacies and private health facilities.

Government policy on tariffs is often guided by broader fiscal and industrial objectives, including revenue mobilisation and efforts to encourage local production of selected goods, including pharmaceuticals.

Malawi has a growing but still limited local pharmaceutical manufacturing sector. Policymakers have previously argued that reducing dependence on imports is key to strengthening domestic industry.

However, many essential medicines, including anti-malarials and antibiotics, continue to be imported to meet national demand.

Malaria remains one of Malawi’s leading public health challenges, while Paracetamol, Ibuprofen and Amoxicillin are among the most widely used medicines in the country.

The development has raised concern among some citizens, who fear the new taxes could make essential medicines less affordable for vulnerable households already facing economic pressure.

The MRA circular took effect immediately upon issuance.

Address

Convection Street
Lilongwe Area 13
PRIVATEBAG388

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when MCP National Youth League posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share