06/08/2026
M’MENE NYENGO IKHALIRE USIKU UNO NDI MAWA PA 7 AUGUST 2026
Tiyembekezere nyengo yozizira kwambiri ndi yopanda mitambo m’madera ambiri usiku uno ndi mawa m’mawa. Chifunga chikhoza kukhalako m’madera ena.
Tiyembekezerenso nyengo ya mitambo yapatalipatali, yofunda ndi yamphepo m’madera ambiri mawa masana.
Chenjezo: Mphepo yamphamvu ya Mwera iziomba pa Nyanja ya Malawi ndi nyanja zina. Choncho, onse ogwiritsa ntchito nyanjazi akhale atcheru poteteza miyoyo ndi katundu.
MPHEPO: Iziomba kuchokera kumwera chakumvuma...
LOWERUKA: Nyengo yamitambo yapatalipatali yofunda ndi ya mphepo…
Mukafuna kudziwa nyengo ya dera lanu pangani dowunilodi apu ya zanyengo (zanyengo app) pa foni yanu ya m'manja yomwe